Genesis 31:38 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndakhala nanu zaka makumi aŵiri tsopano, ndipo nkhosa zanu pamodzi ndi mbuzi zomwe sizidapolozepo ai. Ine sindidadyeko nkhosa za m'khola mwanu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Zaka makumi awiriwo ndakhala nawe, nkhosa ndi mbuzi zako zazikazi sizinapoloze, ndi abira a zoweta zako sindinadye.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Ndakhala nanu kwa zaka makumi awiri tsopano ndipo nkhosa ndi mbuzi zanu sizinapoloze, kapena ine kudyapo nkhosa za mʼkhola mwanu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Zaka makumi awiriwo ndakhala nawe, nkhosa ndi mbuzi zako zazikazi sizinapoloze, ndi abira a zoweta zako sindinadye.