Genesis 31:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nonse aŵirinu mukudziŵa bwino kuti ndidagwira ntchito kwa bambo wanu ndi mphamvu zanga zonse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo inu mudziwa kuti ndi mphamvu zanga zonse ndatumikira atate wanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Inu mukudziwa kuti ndagwirira ntchito abambo anu ndi mphamvu zanga zonse,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo inu mudziwa kuti ndi mphamvu zanga zonse ndatumikira atate wanu.