Genesis 32:27 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthuyo adamufunsa kuti, “Dzina lako ndiwe yani?” Yakobe adayankha kuti, “Dzina langa ndine Yakobe.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo iye anati kwa Yakobo, Dzina lako ndani? Nati iye, Yakobo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu uja anamufunsa Yakobo kuti, “Kodi dzina lako ndiwe yani?” Iye anayankha, “Ndine Yakobo.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo iye anati kwa Yakobo, Dzina lako ndani? Nati iye, Yakobo.