Genesis 34:14 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Iwowo adati, “Sikungatheke kuti tilole mlongo wathu kukwatiwa ndi munthu wosaumbalidwa. Chimenechi ndi chinthu chamanyazi kwa ife.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
nati kwa iwo, Sitingathe kuchita ichi, kupereka mlongo wathu kwa mwamuna wosadulidwa; chifukwa kumeneko ndiko kutichepetsa ife.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwo anati, “Sitingachite zimenezo, kupereka mlongo wathu kwa munthu wosachita mdulidwe. Chimenecho ndi chinthu cha manyazi kwa ife.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
nati kwa iwo, Sitingathe kucita ici, kupereka mlongo wathu kwa mwamuna wosadulidwa; cifukwa kumeneko ndiko kuticepetsa ife.