Genesis 34:17 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma ngati simuvomereza zimene tikunenazi, zoti muumbalidwe, ife tidzangomtenga mwana wathu wamkaziyu.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma mukapanda kutimvera ndi kusadulidwa, pamenepo tidzatenga mwana wathu wamkazi, ndi kumuka naye.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma ngati simuvomereza kuchita mdulidwe titenga mlongo wathu ndi kupita.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma mukapanda kutimvera ndi kusadulidwa, pamenepo tidzatenga mwana wathu wamkazi, ndi kumuka naye.