Genesis 34:18 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mau ameneŵa adakondweretsa kwambiri Hamori ndi mwana wake Sekemu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mau ao ndipo anakomera Hamori ndi Sekemu mwana wake wa Hamori.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mawu amenewa anakondweretsa Hamori ndi mwana wake Sekemu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mau ao ndipo anakomera Hamori ndi Sekemu mwana wace wa Hamori.