Genesis 34:2 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Sekemu, mwana wa Hamori Muhivi, amene anali mfumu ya chigawo cha dzikolo, atamuwona namwaliyo, adamgwira nagona naye.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamene anamuona iye Sekemu, mwana wake wamwamuna wa Hamori Muhivi, kalonga wa dzikolo, anamtenga nagona ndi iye, namuipitsa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamene Sekemu mwana wa Hamori Mhivi, mfumu ya deralo, anamuona, anamugwirira.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamene anamuona iye Sekemu, mwana wace wamwamuna wa Hamori Mhivi, karonga wa dzikolo, anamtenga nagona ndi iye, namuipitsa,