Genesis 34:24 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu amumzindamo adavomereza zimene Hamori ndi Sekemu adanena, ndipo amuna onse amumzindamo adaumbalidwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo onse amene anatuluka pa chipata cha mudzi wao anamvera Hamori ndi mwana wake Sekemu, nadulidwa amuna onse akutuluka pa chipata cha mudzi wao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Amuna onse amene anatuluka ku chipata cha mzinda anavomerezana ndi Hamori ndi mwana wake Sekemu, ndipo aliyense wamwamuna mu mzindamo anachita mdulidwe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo onse amene anaturuka pa cipata ca mudzi wao anamvera Hamori ndi mwana wace Sekemu, nadulidwa amuna onse akuturuka pa cipata ca mudzi wao.