Genesis 34:26 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adapha Hamori ndi mwana wake Sekemu. Adamtenga Dina kumchotsa m'nyumba mwa Sekemu, nachokapo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anapha Hamori ndi Sekemu mwana wake ndi lupanga, natulutsa Dina m'nyumba ya Sekemu nachoka naye.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anapha Hamori ndi Sekemu. Anakatenga Dina ku nyumba kwa Sekemu nanyamuka.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anapha Hamori ndi Sekemu mwana wace ndi lupanga, naturutsa Dina m'nyumba ya Sekemu nacoka naye.