Genesis 34:3 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Sekemu ankamukondadi Dina, mwana wa Yakobe, ndipo ankamulankhula mau achikondi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo mtima wake unakhumba Dina mwana wake wamkazi wa Yakobo, ndipo anamkonda namwaliyo, nanena momkopa namwaliyo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma Sekemu anamukondadi namwali uja, Dina, mwana wa Yakobo motero kuti anamuyankhula mawu womutonthoza.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo mtima wace unakhumba Dina mwana wace wamkazi wa Yakobo, ndipo anamkonda namwaliyo, nanena momkopa namwaliyo.