Genesis 34:31 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma iwowo adati, “Pepani, mlongo wathu sangamusandutse mkazi wachiwerewere ai!”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo iwo anati, Kodi iye ayenera kusandutsa mlongo wathu wadama?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma iwo anayankha kuti, “Pepani, nanga achite kumusandutsa mlongo wathu ngati mkazi wachiwerewere?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo iwo anati, Kodi iye ayenera kusandutsamloogo wathu wadama?