Genesis 34:4 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Choncho adakauza bambo wake kuti, “Nditengereni namwaliyu kuti akhale mkazi wanga.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anati Sekemu kwa atate wake Hamori kuti, Munditengere ine mkazi uyo akhale mkazi wanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Choncho Sekemu anati kwa abambo ake Hamori, “Mundipezere mtsikana uyu kuti akhale mkazi wanga.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anati Sekemu kwa atate wace Hamori kuti, Munditengere ine mkazi uyo akhale mkazi wanga.