Genesis 36:15 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Naŵa mafumu a zidzukulu za Esau. Mwa ana a Elifazi, mwana woyamba wa Esau, panali mafumu aŵa: Temani, Omara, Zefo, Kenazi,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Amenewa ndi mafumu a ana amuna a Esau: ana amuna a Elifazi woyamba wa Esau: mfumu Temani, mfumu Omara, mfumu Zefo, mfumu Kenazi,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nawa mafumu a zidzukulu za Esau: Mwa ana a Elifazi, mwana woyamba wa Esau panali mafumu awa: Temani, Omari, Zefo, ndi Kenazi,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Amenewa ndi mafumu a ana amuna a Esau: ana amuna a Elifazi woyamba wa Esau: mfumu Temani, mfumu Omari, mfumu Zefo, mfumu Kenazi,