Genesis 36:25 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ana a Ana ndi aŵa: Disoni mwana wake wamwamuna, ndi Oholibama mwana wake wamkazi,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ana a Ana ndi awa: Disoni ndi Oholibama mwana wamkazi wa Ana.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ana a Ana anali: Disoni ndi Oholibama mwana wake wamkazi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ana a Ana ndi awa: Disoni ndi Oholibama mwana wamkazi wa Ana.