Genesis 36:30 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Disoni, Ezere ndi Disani. Ameneŵa ndiwo mafumu a Ahori m'dziko la Seiri malinga ndi mafuko ao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
mfumu Disoni, mfumu Ezere, mfumu Disani; amenewa ndi mafumu obadwa kwa Ahori, monga mwa maufumu ao m'dziko la Seiri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Disoni, Ezeri ndi Disani. Amenewa ndiwo mafumu a Ahori, monga mwa mafuko awo, mʼdziko la Seiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
mfumu Disoni, mfumu Ezeri, mfumu Disani; amenewa ndi mafumu obadwa kwa Ahori, monga mwa maufumu ao m'dziko la Seiri.