Genesis 38:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kumeneko Yuda adaonako mtsikana Wachikanani, mwana wa Suwa, namkwatira.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Yuda anaona kumeneko mwana wamkazi wa Mkanani dzina lake Suwa: ndipo anamtenga, nalowa kwa iye.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kumeneko, Yuda anaona mwana wamkazi wa munthu wina wa Chikanaani wotchedwa Suwa. Anamukwatira nagona naye malo amodzi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Yuda anaona kumeneko mwana wamkazi wa Mkanani dzina lace Sua: ndipo anamtenga, nalowa kwa iye.