Genesis 4:13 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kaini adauza Chauta kuti, “Chilango chimenechi nchopitirira mphamvu zanga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Kaini anati kwa Yehova, Kulangidwa kwanga nkwakukulu kosapiririka.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kaini anati kwa Yehova, “Chilango changa ndi chachikulu kuposera mphamvu zanga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Kaini anati kwa Yehova, Kulangidwa kwanga nkwakukuru kosapiririka.