Genesis 4:24 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ngati wopha Kaini amlipsira kasanunkaŵiri, ndiye kuti wopha ine Lameki adzamlipsira kokwanira 77.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ngati Kaini adzabwezeredwa kasanu ndi kawiri, koma Lameki makumi asanu ndi awiri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngati wopha Kaini amulipsira kasanu nʼkawiri, ndiye kuti wopha ine Lameki adzamulipsira kokwanira 77.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ngati Kaini adzabwezeredwa kasanu ndi kawiri, Koma Lameke makumi asanu ndi awiri.