Genesis 4:3 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Patapita nthaŵi, Kaini adatenga zipatso zina zakumunda, nazipereka kwa Chauta.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo panali atapita masiku, Kaini anatenga zipatso za nthaka, nsembe ya kwa Yehova.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Patapita nthawi, Kaini anatenga zipatso za ku munda nakazipereka kwa Yehova monga nsembe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo panali atapita masiku, Kaini anatenga zipatso za nthaka, nsembe ya kwa Yehova.