Genesis 4:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Apo Chauta adafunsa Kainiyo kuti, “Kodi wakwiyiranji chotere? Chifukwa chiyani nkhope yako yagwa?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Yehova anati kwa Kaini, Ukwiyiranji? Yagweranji nkhope yako?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Choncho Yehova anati kwa Kaini, “Chifukwa chiyani wakwiya ndipo bwanji nkhope yako yagwa?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Yehova anati kwa Kaini, Ukwiyiranji? Yagweranji nkhope yako?