Genesis 41:50 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zaka zanjala zisanafike, Yosefe adabereka ana aamuna aŵiri mwa Asenati uja, mwana wa Potifera, wansembe wa ku Oni.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo kwa Yosefe anabadwa ana amuna awiri, chisanafike chaka cha njala, amene Asenati mwana wamkazi wa Potifera wansembe wa Oni anambalira iye.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Zisanafike zaka zanjala, Yosefe anabereka ana aamuna awiri mwa Asenati mwana wa mkazi wa Potifara, wansembe wa Oni.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo kwa Yosefe anabadwa ana amuna awiri, cisanafike caka ca njala, amene Asenati mwana wamkazi wa Porifera wansembe wa Oni anambalira iye.