Genesis 42:13 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono iwowo adati, “Mbuyathu, ife tinalipo ana aamuna khumi ndi aŵiri pachibale pathu, bambo wathu mmodzi, ku dziko la kwathu ku Kanani. Wamng'ono ali ndi bambo wathu, ndipo wina adamwalira.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nati iwo, Akapolo anu ndife abale khumi, ana amuna a munthu mmodzi m'dziko la Kanani; ndipo, taonani, wamng'ono ali ndi atate wathu lero; ndipo palibe mmodzi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma iwo anayankha, “Tinalipo ana aamuna khumi ndi awiri. Abambo athu ndi mmodzi, ndipo kwathu ndi ku Kanaani. Panopo wotsiriza ali ndi abambo athu ndipo wina anamwalira.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nati iwo, Akapolo anu ndife abale khumi, ana amuna a munthu mmodzi m'dziko la Kanani; ndipo, taonani, wamng'ono ali ndi atate wathu lero; ndipo palibe mmodzi.