Genesis 43:19 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Motero asanaloŵe m'nyumbamo adafika kwa wantchito wa Yosefe woyang'anira nyumba uja,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anayandikira kwa tsanyumba wa Yosefe, ndipo ananena ndi iye pa khomo la nyumba, nati,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Choncho atafika pa khomo la nyumba ya Yosefe anamuyandikira wantchito wa Yosefe nayankhula naye kuti,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anayandikira kwa tsanyumba wa Yosefe, ndipo ananena ndi iye pa khomo la nyumba, nati,