Genesis 43:27 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Iye adaŵafunsa m'mene aliri, naŵafunsanso kuti, “Kodi bambo wanu wokalamba uja munkandiwuzayu ali bwanji? Kodi akali moyo?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anafunsa iwo za ubwino wao, nati, Kodi atate wanu ali ndi moyo? Wokalamba uja amene munanena uja: kodi alipo?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yosefe anawafunsa za moyo wawo kenaka anati, “Kodi abambo anu wokalamba amene munkandiwuza aja ali bwanji? Ali ndi moyobe?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anafunsa iwo za ubwino wao, nati, Kodi atate wanu ali ndi moyo? wokalamba uja amene nunanena uja: kodi alipo?