Genesis 44:22 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ife tidaakuyankhani kuti, ‘Mnyamatayo sangachoke kwa bambo wake, popeza kuti akatero, bambo wakeyo kufa kudzakhala komweko.’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ife tinati kwa mbuyanga, Mnyamata sangathei kumsiya atate wake; pakuti akamsiya atate wake, atate wake adzafa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ife tinati, ‘Mbuye wathu, mnyamatayo sangasiye abambo ake, akawasiya ndiye kuti abambo akewo adzafa.’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ife tinati kwa mbuyanga, Mnyamata sangathei kumsiya atate wace; pakuti akamsiya atate wace, atate wace adzafa.