Genesis 44:24 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Titabwerera kwathu kwa bambo wathu mtumiki wanu, tidamuuza mau anu onse aja.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo panali titakwera kunka kwa kapolo wanu atate wanga, tinamfotokozera iye mau a mbuyanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndiye pamene tinafika kwa kapolo wanu, abambo athu tinawawuza zonse zimene munanena.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo panali titakwera kunka kwa kapolo wanus atate, wanga, tinamfotokozera iye mau a mbuyanga.