Genesis 44:27 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma bambo wathu adati, ‘Mukudziŵa kuti mkazi wanga adandibalira ana aŵiri.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo kapolo wanu atate wanga anati kwa ife, Inu mudziwa kuti mkazi wanga anandibalira ine ana amuna awiri;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Koma kapolo wanu, abambo athu anatiwuza kuti, ‘Inu mukudziwa kuti mkazi wanga anandiberekera ana aamuna awiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo kapolo wanu atate wanga anati kwa ife, Inu mudziwa kuti mkazi wanga anandibalira ine ana amuna awiri;