Genesis 44:28 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Wina mwa iwowo adandisiya kale. Ndiye kuti adajiwa ndi zilombo chifukwa sindidamuwonenso.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
wina anatuluka kwa ine ndipo ndinati, Zoonatu, wakadzulidwa; ndipo sindidzamuonanso iye;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mmodzi wa iwo anandisiya. Ine ndimati anadyedwa ndi chirombo popeza sindinamuonenso mpaka lero.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
wina anaturuka kwa ine ndipo ndinati, Zoonatu, wakadzulidwa; ndipo sindidzamuonanso iye;