Genesis 44:3 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
M'maŵa kutacha, anthu aja adaloledwa kupita pamodzi ndi abulu ao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamene kudacha, anamukitsa anthu iwo ndi abulu ao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mmawa kutacha anthu aja analoledwa kuti apite ndi abulu awo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamene kudaca, anamukitsa anthu iwo ndi aburu ao.