Genesis 44:33 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndiye tsopano bwana, ineyo nditsalira kuno kuti ndikhale kapolo wanu m'malo mwa mnyamatayu. Muloleni iyeyu apite ndi abale akeŵa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Tsopanotu, mtumiki wanu akhale kapolo wa mbuyanga m'malo mwa mnyamata; mnyamatayo akwere pamodzi ndi abale ake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Tsono, chonde mulole kuti ine kapolo wanu nditsalire kuno kukhala kapolo wa mbuye wathu mʼmalo mwa mnyamatayu. Koma iye apite pamodzi ndi abale akewa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Tsopanotu, mtumiki wanu akhale kapolo wa mbuyanga m'malo mwa mnyamata; mnyamatayo akwere pamodzi ndi abale ace.