Genesis 47:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yosefe adaŵayankha kuti “Bwerani ndi zoŵeta zanu, tidzasinthane ndi chakudya, ngati mukuti ndalama zanu zidatha zonse.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Yosefe anati, Mundipatse ng'ombe zanu: ndipo ndidzakupatsani inu mtengo wa ng'ombe zanu ngati ndalama zatsirizika.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo Yosefe anawayankha kuti, “Bwerani ndi ziweto zanu ndipo tidzasinthana ndi chakudya poti mukuti ndalama zanu zatha.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Yosefe anati, Mundipatse ng'ombe zanu: ndipo ndidzakupatsani inu mtengo wa ng'ombe zanu ngati ndalama zatsirizika.