Genesis 47:27 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Aisraele atakhazikika ku Ejipito, adalemera kwambiri, ndipo adaberekanso ana ambiri.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Israele anakhala m'dziko la Ejipito, m'dziko la Goseni; nakhala nazo zaozao m'menemo, nabalana nachuluka kwambiri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsono Aisraeli anakhazikika mʼdziko la Igupto ku chigawo cha Goseni. Kumeneko anapeza chuma ndipo anaberekana nachuluka kwambiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Israyeli anakhala m'dziko la Aigupto, m'dziko la Goseni; nakhala nazo zaozao m'menemo, nabalana nacuruka kwambiri.