Genesis 48:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yakobe ataona ana a Yosefe, adafunsa kuti, “Nanga anyamata aŵa nga yani?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Israele anayang'ana ana amuna a Yosefe, nati, Ndani awa?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Israeli ataona ana a Yosefe anafunsa kuti, “Anyamatawa ndi a yani?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Israyeli anayang'ana ana amuna a Yosefe, nati, Ndani awa?