Genesis 49:16 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Dani adzalamulira anthu ake. Anthuwo adzalingana ndi mafuko ena a Israele.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Dani adzaweruza anthu ake, monga limodzi la mafuko a Israele.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Dani adzaweruza mwachilungamo anthu ake monga limodzi mwa mafuko a anthu a mu Israeli.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Dani adzaweruza anthu ace, Monga limodzi la mafuko a Israyeli.