Genesis 49:21 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Nafutali ali ngati insa yongoyenda mwaufulu, imene imabala ana okongola.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nafutali ndi mbawala yomasuka; apatsa mau abwino.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Nafutali ali ngati mbawala yayikazi yokhala ndi ana okongola kwambiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nafitali ndi nswala yomasuka; Apatsa mau abwino.