Genesis 49:32 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mundawo pamodzi ndi phangalo adagula kwa Ahiti.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
munda ndi phanga lili m'menemo, zinagulidwa kwa ana a Hiti
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munda ndi manda amene ali mʼmenemo zinagulidwa kwa Ahiti.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
munda ndi phanga liri m'menemo, zinagulidwa kwa ana a Heti.