Genesis 5:12 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kenani ali wa zaka 70, adabereka mwana dzina lake Mahalalele,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Kenani anakhala ndi moyo zaka makumi asanu ndi awiri, ndipo anabala Mahalalele:
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamene Kenani anali ndi zaka 70, anabereka Mahalaleli.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Kenani anakhala ndi moyo zaka makumi asanu ndi awiri, ndipo anabala Mahalalele: