Genesis 5:9 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Enosi ali wa zaka 90, adabereka mwana dzina lake Kenani,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Enosi anakhala ndi moyo zaka makumi asanu ndi anai, nabala Kenani;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamene Enosi anali ndi zaka 90, anabereka Kenani.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Enosi anakhala ndi moyo zaka makumi asanu ndi anai, nabala Kenani;