Genesis 50:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Motero adatumiza mau kwa Yosefe kuti, “Atate anu asanafe adanena mau akuti,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anatumiza mthenga kwa Yosefe kuti, Atate wathu asanafe analamulira, kuti,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Motero anatumiza mawu kwa Yosefe kuti, “Abambo anu anasiya malangizo asanafe nati:
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anatumiza mthenga kwa Yosefe kuti, Atate wathu asanafe analamulira, kuti,