Genesis 7:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Patangopita masiku asanu ndi aŵiri, chigumula chidafika pa dziko lonse lapansi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo panali pamene anapita masiku asanu ndi awiri, madzi a chigumula anali pa dziko lapansi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Patapita masiku asanu ndi awiri chigumula chinabwera pa dziko lapansi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo panali pamene anapita masiku asanu ndi awiri, madzi a cigumula anali pa dziko lapansi.