Genesis 7:19 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kukwera kwa madzi kudapitirira ndithu mpaka kumiza ndi mapiri aatali omwe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo madzi anapambana ndithu pa dziko lapansi; anamizidwa mapiri aatali onse amene anali pansi pa thambo lonse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Madzi a chigumula anabwerabe molimbika motero kuti mapiri ataliatali onse a pa dziko anamizidwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo madzi anapambana ndithu pa dziko lapansi; anamizidwa mapiri atari onse amene anali pansi pa thambo lonse.