Genesis 7:20 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono adakwererakwerera ndithu mpaka kubzola nsonga za mapiriwo mamita asanu ndi aŵiri.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Madzi anapambana ndithu nakwera mikono khumi ndi isanu: namizidwa mapiri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Madzi anakwera namiza mapiri kwa mamita pafupifupi asanu ndi awiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Madzi anapambana ndithu nakwera mikono khumi ndi isanu: namizidwa mapiri,