Genesis 7:24 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Madziwo adakhala osaphwa konse pa dziko lapansi masiku 150.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anapambana madzi pa dziko lapansi masiku zana kudza makumi asanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Madziwo anadzaza dziko lonse lapansi kwa masiku 150.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anapambana madzi pa dziko lapansi masiku zana kudza makumi asanu.