Genesis 7:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nowa anali wa zaka 600 pamene chigumulacho chidafika pa dziko lapansi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Nowa anali wa zaka mazana asanu ndi limodzi, pamene chigumula cha madzi chinali pa dziko lapansi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamene chigumula chinabwera pa dziko lapansi Nowa anali ndi zaka 600.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Nowa anali wa zaka mazana asanu ndi limodzi, pamene cigumula ca madzi cinali pa dziko lapansi.