Genesis 7:9 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nowa adaloŵa nazo m'chombo, monga Mulungu adaalamulira.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
zinalowa ziwiriziwiri kwa Nowa m'chingalawamo, yamphongo ndi yaikazi, monga momwe Mulungu anamlamulira Nowa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo Nowa anatenga ziwiriziwiri, yayimuna ndi yayikazi monga anamulamulira Mulungu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
zinalowa ziwiri ziwiri kwa Nowa m'cingalawamo, yamphongo ndi yaikazi, monga momwe Mulungu anamlamulira Nowa.