Genesis 9:19 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ana a Nowa atatu ameneŵa ndiwo makolo a anthu a pa dziko lonse lapansi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Amenewa ndiwo ana amuna atatu a Nowa: ndiwo anafalikira dziko lonse lapansi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ana aamuna a Nowa amenewa ndiwo anali makolo a anthu onse pa dziko lapansi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Amenewa ndiwo ana amuna atatu a Nowa: ndiwo anafalikira dziko lonse lapansi.