Genesis 9:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nowa anali mlimi ndipo anali woyamba kulima munda wamphesa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anayamba Nowa kukhala munthu wakulima nthaka, ndipo analima munda wamphesa:
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nowa anali munthu woyamba kulima munda wamphesa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anayamba Nowa kukhala munthu wakulima nthaka, ndipo analima munda wamphesa: