Genesis 9:21 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsiku lina atangomwa vinyo, adaledzera, ndipo adavula zovala zake zonse, nakagona ali maliseche m'hema mwake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
namwa vinyo wake, naledzera; ndipo anali wamaliseche m'kati mwa hema wake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsiku lina pamene Nowa anamwako vinyo wa zipatso za mʼmundawo analedzera ndipo anavula zovala zake zonse ndi kugona mu tenti yake ali maliseche.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
namwa vinyo wace, naledzera; ndipo anali wamarisece m'kati mwa bema wace.