Genesis 9:24 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nowa atadzuka, adamva zonse zimene mwana wake wamng'onoyo adaachita,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nowa ndipo anauka kwa kuledzera kwake, nadziwa chimene anamchitira iye mwana wake wamng'ono.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nowa atadzuka, kuledzera kutatha, ndikudziwa zimene mwana wake wamngʼono wamwamuna uja anamuchitira,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nowa ndipo anauka kwa kuledzera kwace, nadziwa cimene anamcitira iye mwana wace wamng'ono.