Genesis 9:25 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
ndipo adati, “Atembereredwe Kanani! Adzakhala kapolo weniweni wa abale ake.” Popitiriza mau adati,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anati, Wotembereredwa ndi Kanani; adzakhala kwa abale ake kapolo wa akapolo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
anati, “Atembereredwe Kanaani! Adzakhala kapolo wa pansi kwenikweni kwa abale ake.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anati, Wotembereredwa ndi Kanani: Adzakhala kwa abale ace kapolo wa akapolo: